Ntano ya Nyemba
Nina Orange
Nina Orange

Munzanga ananipasa nyemba zomwe anakolola mumunda wake.

1

Nishanga nyemba mudothi.

2

Nyemba yayamba kuphukila mu dothi.

3

M'mela pokula upita kumwamba kuzuba. Mizu zimela kungena mudothi.

4

M'mela utuluka pamwamba pa nthaka.

5

M'mela uyamba kukula,

6

Na kukula.

7

Nishanganso zina nyemba.

8

Nyemba zikula,

9

Na kukula.

10

Nyemba zamela makoko.

11

Nyemba zakula kupita kumwamba, na kumwamba kukwela cipupa.

12

Nikolola makoko akayuma.

13

Nicosa nyemba mu makoko.

14

Niphika nyemba, kuphikila pamodzi na anyezi ni ma spaici ena.

15

Izi nyemba zapya kuti tidye.

16
You are free to download, copy, translate or adapt this story and use the illustrations as long as you attribute in the following way:
Ntano ya Nyemba
Author - Nina Orange
Translation - Bether Mwale-Moyo, Moffat Moyo
Illustration - Nina Orange
Language - CiNyanja
Level - First words